Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 104:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Zonsezi zimayembekezera inu+

      Kuti muzipatse chakudya pa nyengo yake.+

  • Salimo 147:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Iye amapatsa zilombo chakudya chawo,+

      Amapatsanso ana a makwangwala chakudya chimene amalirira.+

  • Mateyu 6:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Onetsetsani mbalame+ zam’mlengalenga, pajatu sizifesa mbewu kapena kukolola, kapenanso kusunga chakudya m’nkhokwe. Koma Atate wanu wakumwamba amazidyetsa. Nanga inu sindinu amtengo wapatali kuposa mbalame kodi?+

  • Luka 12:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Onetsetsani makwangwala,+ iwo safesa mbewu kapena kukolola. Alibe nyumba yosungiramo zinthu kapena nkhokwe, komatu Mulungu amawadyetsa. Kodi inu si ofunika kwambiri kuposa mbalame?+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena