Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 12:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Ali pafupi kulowa mu Iguputo, anauza mkazi wake Sarai kuti: “Ndikudziwa ndithu kuti ndiwe mkazi wokongola m’maonekedwe ako.+

  • Genesis 17:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Ndiyeno Mulungu anauza Abulahamu kuti: “Sarai mkazi wako usamutchulenso kuti Sarai, chifukwa tsopano dzina lake ndi Sara.+

  • Genesis 20:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Komabe, ndi mlongo wangadi ameneyu. Bambo athu ndi amodzi, tinangosiyana mayi, ndipo ndinam’kwatira.+

  • 1 Petulo 3:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 monga mmene Sara analili womvera kwa Abulahamu, ndipo anali kumutcha kuti “mbuyanga.”+ Tsopano inuyo mwakhala ana ake, ndipo mukhalabe ana ake mukapitiriza kuchita zabwino ndi kusaopa chochititsa mantha chilichonse.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena