Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 110:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Yehova walumbira+ (ndipo sadzasintha maganizo). Iye wati:+

      “Iwe ndiwe wansembe mpaka kalekale,+

      Monga mwa unsembe wa Melekizedeki!”+

  • Aheberi 6:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 kumene Yesu, yemwe ndi kalambulabwalo anakalowa chifukwa cha ife.+ Iyeyu wakhala mkulu wa ansembe mpaka muyaya monga mwa unsembe wa Melekizedeki.+

  • Aheberi 7:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Popeza kuti analibe bambo, analibe mayi, analibe mzere wa mibadwo ya makolo ndipo tsiku limene anabadwa+ komanso limene anamwalira silikudziwika, koma anamuchititsa kuti afanane ndi Mwana wa Mulungu,+ iye ndi wansembe kwamuyaya.+

  • Aheberi 7:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Izi zinachitika m’njira yakuti iye anali adakali m’chiuno+ mwa kholo lake pamene Melekizedeki anakumana ndi kholo lakelo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena