-
Ekisodo 37:19Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
19 Pamalo atatu a nthambi za mbali imodzi, panali masamba ofunga duwa opangidwa ngati maluwa a mtengo wa amondi, ndipo masambawo anatsatizana ndi mfundo ndi maluwa. Pamalo atatu a nthambi za mbali inayo, panalinso masamba ofunga duwa opangidwa ngati maluwa a mtengo wa amondi, ndipo masambawo anatsatizana ndi mfundo ndi maluwa. Nthambi 6 zotuluka m’choikapo nyalecho zinali zotero.+
-