2 “Tenga Aroni pamodzi ndi ana ake,+ zovala zawo,+ mafuta odzozera,+ ng’ombe yamphongo ya nsembe yamachimo,+ nkhosa ziwiri zamphongo, ndi dengu la mikate yopanda chofufumitsa.+
5Mkulu wa ansembe aliyense wotengedwa mwa anthu amaikidwa kuti achite utumiki wa Mulungu m’malo mwa anthu,+ kuti azipereka mphatso ndi nsembe zophimba machimo.+