Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 58:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Koma tsiku ndi tsiku iwo anali kufunafuna ineyo. Anali kunena kuti amasangalala kudziwa njira zanga,+ ngati mtundu umene unali kuchita zolungama ndiponso ngati mtundu umene sunasiye chilungamo cha Mulungu wawo.+ Iwo ankangokhalira kundipempha chiweruzo cholungama, ndipo anali kuyandikira kwa Mulungu amene anali kumukonda.+

  • Yohane 8:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Koma ndikati ndiweruze, chiweruzo changa chimakhala cholungama, chifukwa sindiweruza ndekha, pakuti Atate amene anandituma ali ndi ine.+

  • Aheberi 4:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Pakuti mkulu wa ansembe amene tili naye si mkulu wa ansembe amene sangatimvere chisoni+ pa zofooka zathu. Koma tili ndi mkulu wa ansembe amene anayesedwa m’zonse ngati ifeyo, ndipo anakhalabe wopanda uchimo.+

  • Aheberi 5:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Mkulu wa ansembe aliyense wotengedwa mwa anthu amaikidwa kuti achite utumiki wa Mulungu m’malo mwa anthu,+ kuti azipereka mphatso ndi nsembe zophimba machimo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena