Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 28:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Ndipo iwe ulankhule ndi anthu onse aluso amene ndinadzaza mzimu wa nzeru+ m’mitima yawo kuti amupangire Aroni zovala zomuyeretsa, kuti atumikire monga wansembe wanga.+

  • Ekisodo 31:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Ndipo inetu ndaika Oholiabu mwana wamwamuna wa Ahisama wa fuko la Dani+ kuti athandize Bezaleli. Komanso ndaika nzeru mumtima wa munthu aliyense waluso, kuti apange zonse zimene ndakulamulazi:+

  • Ekisodo 35:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 “‘Onse aluso+ pakati panu abwere ndi kupanga zinthu zonse zimene Yehova walamula.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena