Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 20:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 “Ine ndine Yehova Mulungu wako,+ amene ndinakutulutsa m’dziko la Iguputo, m’nyumba yaukapolo.+

  • Levitiko 25:43
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 43 Musamupondereze ndi kumuchitira nkhanza,+ ndipo muziopa Mulungu wanu.+

  • Levitiko 26:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Ine ndine Yehova Mulungu wanu, amene ndinakutulutsani m’dziko la Iguputo kuti musakhale akapolo a Aiguputo.+ Ndinathyola goli lanu ndi kukuchititsani kuyenda mowongoka.+

  • Miyambo 29:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Olungama akachuluka, anthu amasangalala,+ koma aliyense woipa akayamba kulamulira, anthu amabuula.+

  • Yesaya 14:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 amene anali kumenya mwaukali anthu a mitundu yosiyanasiyana powakwapula mosalekeza,+ ndiponso amene anali kugonjetsa mitundu ya anthu mokwiya, ndi chizunzo chopanda malire.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena