Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 4:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Kenako Mose anatenga mkazi wake ndi ana ake ndi kuwakweza pabulu, ndi kuyamba ulendo wobwerera ku Iguputo. Komanso, Mose anatenga ndodo ya Mulungu woona m’dzanja lake.+

  • Ekisodo 17:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Zitatero Mose anauza Yoswa* kuti:+ “Tisankhire amuna, ndipo upite nawo+ kukamenyana ndi Aamaleki. Mawa ndikaima pamwamba pa phiri nditagwira ndodo ya Mulungu woona m’dzanja langa.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena