-
Levitiko 14:6Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
6 Koma azitenga mbalame inayo pamodzi ndi nthambi ya mtengo wa mkungudza, ulusi wofiira kwambiri ndi kamtengo ka hisope, n’kuziviika pamodzi ndi mbalame yamoyo ija m’magazi a mbalame imene aiphera pamwamba pa madzi otunga kumtsinje ija.
-