Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 11:31
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 31 Kenako Yehova anautsa mphepo+ yamkokomo kuchokera kunyanja. Mphepoyo inabweretsa zinziri,+ ndipo inazimwaza kuyambira pamsasapo mpaka pamtunda woyenda tsiku limodzi kulowera mbali ina, ndiponso mtunda woyenda tsiku limodzi kulowera mbali inayo. Inazimwaza kuzungulira msasawo, moti zinali kuuluka m’munsi kwambiri pafupifupi mikono* iwiri kuchokera pansi.

  • Salimo 78:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Iye anagwetsa chakudya pa iwo ngati fumbi.+

      Anawagwetsera zolengedwa zamapiko zouluka, zochuluka ngati mchenga wakunyanja.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena