Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 20:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 muzichita ntchito zanu zonse masiku 6.+

  • Ekisodo 31:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 “Koma iwe uuze ana a Isiraeli kuti, ‘Muonetsetse kuti muzisunga masiku anga a sabata,+ pakuti ndi chizindikiro pakati pa ine ndi inu m’mibadwo yanu yonse, kuti mudziwe kuti ine Yehova ndakusankhani kukhala opatulika.+

  • Deuteronomo 5:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Uzikumbukira kuti unali kapolo m’dziko la Iguputo+ ndipo Yehova Mulungu wako anakutulutsa kumeneko ndi dzanja lamphamvu ndi mkono wotambasula.+ N’chifukwa chake Yehova Mulungu wako anakulamula kuti uzisunga tsiku la sabata.+

  • Yeremiya 17:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Musatulutse katundu aliyense kuchokera m’nyumba zanu pa tsiku la sabata ndipo musamagwire ntchito iliyonse.+ Tsiku la sabata muziliona kukhala lopatulika monga mmene ndinalamulira makolo anu.+

  • Mateyu 12:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Komatu munthu ndi wofunika kwambiri kuposa nkhosa.+ Choncho, n’kololeka inde kuchita chinthu chabwino pa tsiku la sabata.”

  • Luka 13:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Koma Ambuye anamuyankha kuti: “Onyenga inu,+ kodi aliyense wa inu samasula ng’ombe yake kapena bulu wake m’khola pa sabata ndi kupita naye kukam’mwetsa madzi?+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena