-
Yobu 11:19Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
19 Ndithu udzadziwongola popanda aliyense wokuopsa.
Anthu ambiri adzakupangira zinthu zokuchititsa kuwakomera mtima.+
-
Yeremiya 30:10Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
10 “Koma iwe Yakobo mtumiki wanga usachite mantha, iwe Isiraeli usagwidwe ndi mantha,”+ watero Yehova. “Pakuti ine ndikukupulumutsa kuchokera kutali ndipo ndikupulumutsanso ana ako kuchokera kudziko limene anatengedwa kukakhala akapolo.+ Yakobo adzabwerera ndipo adzakhala mosatekeseka komanso mopanda zosokoneza. Sipadzakhala womuopsa.”+
-
-
-