Levitiko 4:5 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 5 Pamenepo wansembe, wodzozedwayo,+ azitengako pang’ono magazi a ng’ombeyo ndi kulowa nawo m’chihema chokumanako. Levitiko 10:18 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 18 Taonani, simunabweretse magazi ake mkati, m’malo oyera.+ Munafunika kudya nsembeyo m’malo oyera, monga mmene Mulungu anandilamulira.”+ Levitiko 16:27 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 27 “Koma ng’ombe yamphongo ya nsembe yamachimo ndi mbuzi ya nsembe yamachimo zimene magazi ake analowa nawo m’malo oyera pokaphimba machimo, azizitulutsira kunja kwa msasa ndipo azitentha pamoto zikopa zake, nyama ndi ndowe zake.+ Aheberi 13:11 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 11 Pakuti nyama zimene magazi ake, mkulu wa ansembe amalowa nawo m’malo oyera chifukwa cha machimo, amakazitentha kunja kwa msasa.+
5 Pamenepo wansembe, wodzozedwayo,+ azitengako pang’ono magazi a ng’ombeyo ndi kulowa nawo m’chihema chokumanako.
18 Taonani, simunabweretse magazi ake mkati, m’malo oyera.+ Munafunika kudya nsembeyo m’malo oyera, monga mmene Mulungu anandilamulira.”+
27 “Koma ng’ombe yamphongo ya nsembe yamachimo ndi mbuzi ya nsembe yamachimo zimene magazi ake analowa nawo m’malo oyera pokaphimba machimo, azizitulutsira kunja kwa msasa ndipo azitentha pamoto zikopa zake, nyama ndi ndowe zake.+
11 Pakuti nyama zimene magazi ake, mkulu wa ansembe amalowa nawo m’malo oyera chifukwa cha machimo, amakazitentha kunja kwa msasa.+