Levitiko 5:13 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 13 Ndiyeno wansembeyo aziphimba+ tchimo limene munthuyo wachita. Aziphimba tchimo lililonse mwa machimo amenewa, ndipo azikhululukidwa. Ufa wotsalawo uzikhala wa wansembe+ mofanana ndi nsembe yambewu.’” Levitiko 6:16 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 16 Aroni ndi ana ake azidya zotsala za nsembe imeneyi.+ Azipanga mkate wopanda chofufumitsa+ ndi kudya mkatewo m’malo oyera. Aziudyera m’bwalo la chihema chokumanako. Levitiko 8:29 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 29 Kenako Mose anatenga nganga+ ndi kuiweyula uku ndi uku monga nsembe yoweyula yoperekedwa kwa Yehova.+ Nganga imeneyi anaitenga pa nkhosa yowalongera unsembe ndipo inakhala gawo+ la Mose, monga mmene Yehova analamulira Mose. Numeri 18:18 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 18 Uzitenga nyama yake kuti ikhale yako, mofanana ndi nganga ya nsembe yoweyula, komanso mwendo wam’mbuyo wakumanja.+
13 Ndiyeno wansembeyo aziphimba+ tchimo limene munthuyo wachita. Aziphimba tchimo lililonse mwa machimo amenewa, ndipo azikhululukidwa. Ufa wotsalawo uzikhala wa wansembe+ mofanana ndi nsembe yambewu.’”
16 Aroni ndi ana ake azidya zotsala za nsembe imeneyi.+ Azipanga mkate wopanda chofufumitsa+ ndi kudya mkatewo m’malo oyera. Aziudyera m’bwalo la chihema chokumanako.
29 Kenako Mose anatenga nganga+ ndi kuiweyula uku ndi uku monga nsembe yoweyula yoperekedwa kwa Yehova.+ Nganga imeneyi anaitenga pa nkhosa yowalongera unsembe ndipo inakhala gawo+ la Mose, monga mmene Yehova analamulira Mose.
18 Uzitenga nyama yake kuti ikhale yako, mofanana ndi nganga ya nsembe yoweyula, komanso mwendo wam’mbuyo wakumanja.+