Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Levitiko 7:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 “Uza ana a Isiraeli kuti, ‘Musamadye mafuta+ alionse a ng’ombe, a mwana wa nkhosa, kapena a mbuzi.

  • 1 Samueli 2:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Wopereka nsembeyo akanena kuti: “Yembekeza kaye apsereze mafutawo,+ kenako utenge chilichonse chimene mtima wako ukufuna,”+ iye anali kuyankha kuti: “Ayi, ndipatse pompano, ukapanda kundipatsa, ndichita kulanda!”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena