Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Levitiko 21:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Yehova anapitiriza kulankhula ndi Mose kuti: “Uza ansembe, ana a Aroni, kuti, ‘Aliyense wa inu asadziipitse chifukwa cha munthu amene wamwalira pakati pa anthu a mtundu wake.*+

  • Levitiko 21:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Iye asayandikire munthu wakufa+ ndipo asadziipitse bambo ndi mayi ake akamwalira.

  • Numeri 5:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 “Lamula ana a Isiraeli kuti azitulutsa mumsasa munthu aliyense wakhate,+ aliyense wakukha kumaliseche,+ ndi aliyense wodetsedwa chifukwa chokhudza mtembo wa munthu.+

  • Numeri 6:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Koma ngati munthu wina wafera pambali pake mwadzidzidzi,+ moti Mnaziriyo waipitsa mutu umene uli ndi chizindikiro cha unaziri wake pokhudza mtembowo, amete tsitsi+ la kumutu kwake pa tsiku la kuyeretsedwa kwake. Alimete pa tsiku la 7.

  • Numeri 9:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Tsopano panali amuna ena amene anadzidetsa pokhudza mtembo wa munthu,+ moti sanathe kukonza nsembe ya pasika pa tsikulo. Chotero anakaonekera kwa Mose ndi Aroni pa tsikulo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena