Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 22:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Tsopano iye anatumiza amithenga kwa Balamu,+ mwana wa Beori, ku Petori+ pafupi ndi Mtsinje*+ wa m’dziko lawo. Anawatuma kuti akamuitane, kuti: “Taonani! Anthu ochokera ku Iguputo afika kuno. Iwo adzaza dziko lino kulikonse kumene munthu angayang’ane,+ ndipo akukhala pafupi penipeni moyang’anana ndi ine.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena