Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 38:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Anaberekanso mwana wina wamwamuna n’kumutcha dzina lakuti Shela. Mwana ameneyu anam’bereka ali ku Akizibu. +

  • Genesis 38:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Ndiyeno Yuda ataziyang’anitsitsa, ananena kuti:+ “Mkaziyu ndi wolungama koposa ine,+ chifukwa sindinam’pereke kwa mwana wanga Shela.”+ Zitatero, Yuda sanagone nayenso.+

  • 1 Mbiri 4:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Ana a Shela+ mwana wa Yuda anali Ere bambo wa Leka, Laada bambo wa Maresha, ndi mabanja a nyumba ya anthu ogwira ntchito yopanga nsalu zabwino kwambiri,+ a nyumba ya Asibeya,

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena