Deuteronomo 19:11 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 11 “Koma pakakhala munthu wodana+ ndi mnzake amene wabisalira ndi kuukira mnzakeyo panjira n’kumukantha ndipo wafa,+ iye n’kuthawira ku umodzi mwa mizinda imeneyi, Deuteronomo 19:12 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 12 akulu a mumzinda wakwawo azitumiza anthu kukam’tenga kumeneko, ndipo azim’pereka m’manja mwa wobwezera magazi kuti afe ndithu.+ Yoswa 20:5 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 5 Ngati wobwezera magazi atam’thamangitsa, akuluwo asapereke wopha munthuyo m’manja mwa wobwezera magaziyo,+ chifukwa iye sanaphe munthu mnzakeyo mwadala, ndiponso sankadana naye.+
11 “Koma pakakhala munthu wodana+ ndi mnzake amene wabisalira ndi kuukira mnzakeyo panjira n’kumukantha ndipo wafa,+ iye n’kuthawira ku umodzi mwa mizinda imeneyi,
12 akulu a mumzinda wakwawo azitumiza anthu kukam’tenga kumeneko, ndipo azim’pereka m’manja mwa wobwezera magazi kuti afe ndithu.+
5 Ngati wobwezera magazi atam’thamangitsa, akuluwo asapereke wopha munthuyo m’manja mwa wobwezera magaziyo,+ chifukwa iye sanaphe munthu mnzakeyo mwadala, ndiponso sankadana naye.+