Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 6:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 “Lankhula ndi ana a Isiraeli, ndipo uwauze kuti, ‘Munthu aliyense, mwamuna kapena mkazi, akachita lonjezo lapadera lokhala Mnaziri+ kwa Yehova,

  • Oweruza 13:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Pakuti udzatenga pakati ndi kubereka mwana wamwamuna. M’mutu mwake musadzadutse lezala+ chifukwa mwanayo adzakhala Mnaziri+ wa Mulungu potuluka m’mimba.+ Iye adzakhala patsogolo populumutsa Isiraeli m’manja mwa Afilisiti.”+

  • Oweruza 16:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Pamapeto pake, Samisoni anamuululira zonse za pansi pa mtima wake,+ kuti: “M’mutu mwanga simunadutsepo lezala,+ chifukwa ndine Mnaziri wa Mulungu kuyambira ndili m’mimba mwa mayi anga.+ Atandimeta, mphamvu zanga zikhoza kundichokera, ndipo ndingafooke ndi kukhala ngati anthu ena onse.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena