Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 1:33
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 33 amene anali kutsogola kuti akuzondereni malo oti mumangepo msasa wanu.+ Usiku anali kukutsogolerani ndi moto kuti muziona njira yoyendamo, ndipo masana anali kukutsogolerani ndi mtambo.+

  • Yoswa 3:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 ndipo anauza anthuwo kuti: “Mukangoona likasa la pangano la Yehova Mulungu wanu litanyamulidwa ndi ansembe achilevi,+ musamuke pamalo panu ndi kulitsatira,

  • Yoswa 3:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 koma musaliyandikire. Pakati pa inu ndi likasalo pakhale mtunda wokwana mikono* pafupifupi 2,000.+ Mukatero, mudzadziwa njira yoyenera kuyendamo, pakuti kumeneko simunayambe mwapitako.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena