Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 16:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Aliyense akatenge chofukizira chake. Mukaikemo nsembe yofukiza, ndipo aliyense adzabweretse chofukizira chake pamaso pa Yehova. Zofukizirazo zidzakhalepo zokwanira 250, komanso iweyo ndi Aroni aliyense adzakhale ndi chake.”

  • Numeri 26:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Zitatero, nthaka inayasama n’kuwameza.+ Koma Kora anafa pamene moto unanyeketsa gulu la amuna 250.+ Choncho iwowa anakhala chitsanzo chopereka chenjezo.+

  • Salimo 106:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Moto unayaka pakati pa msonkhano wawo.+

      Malawi amoto ananyeketsa anthu oipawo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena