-
Ekisodo 28:38Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
38 Chotero kachitsuloko kazikhala pamphumi pa Aroni, ndipo Aroni aziyankha mlandu wa machimo ochimwira zinthu zopatulika,+ zimene ana a Isiraeli adzaziyeretsa. Izi ndizo mphatso zawo zonse zopatulika. Kachitsuloko kazikhala pamphumi pake nthawi zonse, kuti azichititsa anthuwo kukhala ovomerezeka+ pamaso pa Yehova.
-