Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Samueli 22:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Ndidzakhalabe wopanda cholakwa+ pamaso pake,

      Ndipo ndidzayesetsa kupewa cholakwa.+

  • Salimo 37:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Yehova amadziwa za moyo wa anthu osalakwa,+

      Ndipo cholowa chawo chidzakhalapo mpaka kalekale.+

  • Mateyu 5:48
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 48 Choncho khalani angwiro, monga mmene Atate wanu wakumwamba alili wangwiro.+

  • 2 Petulo 3:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Chotero okondedwa, pakuti mukuyembekezera zinthu zimenezi, chitani chilichonse chotheka kuti iye adzakupezeni opanda banga,+ opanda chilema ndiponso muli mu mtendere.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena