Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 25:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Pakuti aliyense wochita zimenezi, aliyense wosachita chilungamo, n’ngonyansa kwa Yehova Mulungu wako.+

  • Yobu 34:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Choncho inu amuna a mtima+ womvetsa zinthu, ndimvereni.

      Mulungu woona sangachite zoipa m’pang’ono pomwe,+

      Ndipo Wamphamvuyonse sangachite zinthu zopanda chilungamo ngakhale pang’ono.+

  • Aroma 3:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Komabe, ngati kulungama kwa Mulungu+ kukuonekera chifukwa cha kusalungama kwathu, ndiye tinene kuti chiyani? Kodi tingati Mulungu ndi wosalungama+ poonetsa mkwiyo wake? (Ndikulankhula mmene anthu+ amalankhulira.)

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena