Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 18:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Simungachite zimenezo, kupha munthu wolungama limodzi ndi woipa. Sizingatheke kuti wolungama aone zofanana ndi woipa.+ Simungachite zimenezo ayi.+ Kodi Woweruza wa dziko lonse lapansi sadzachita cholungama?”+

  • Salimo 92:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Kuti alengeze kuti Yehova ndi wolungama.+

      Iye ndi Thanthwe langa,+ ndipo sachita zosalungama.+

  • Salimo 99:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Iye amakonda chilungamo ngati mmene mfumu yamphamvu imachitira.+

      Inu mwakhazikitsa kulungama.+

      Mwakhazikitsa chiweruzo ndi chilungamo pakati pa ana a Yakobo.+

  • Hoseya 14:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Ndani ali ndi nzeru kuti amvetse zinthu zimenezi?+ Wochenjera ndani kuti adziwe zimenezi?+ Pakuti njira za Yehova ndi zowongoka+ ndipo anthu olungama ndi amene adzayendamo,+ koma olakwa adzapunthwa m’njira zimenezo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena