Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 6:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Ndipo mawu awa amene ndikukulamula lero azikhala pamtima pako,+

  • Salimo 37:31
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 31 Chilamulo cha Mulungu wake chili mumtima mwake.+

      Poyenda mapazi ake sadzaterereka.+

  • Miyambo 7:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Uwamange kuzala zako,+ ndipo uwalembe pamtima pako.+

  • Yesaya 51:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 “Ndimvereni, inu odziwa chilungamo, inu amene muli ndi lamulo langa mumtima mwanu.+ Musaope chitonzo cha anthu ndipo musachite mantha chifukwa cha mawu awo onyoza.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena