Genesis 46:11 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 11 Ana a Levi+ anali Gerisoni,+ Kohati+ ndi Merari.+ Numeri 3:27 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 27 Mwa ana a Kohati, panali banja la Aamuramu, banja la Aizara, banja la Aheburoni ndi banja la Auziyeli. Awa ndiwo anali mabanja a Akohati.+ Numeri 3:28 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 28 Amuna onse owerengedwa, kuyambira amwezi umodzi kupita m’tsogolo, analipo 8,600. Ntchito ya amenewa inali kutumikira pamalo oyera.+ Numeri 3:31 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 31 Ntchito yawo+ inali yosamalira likasa,+ tebulo,+ choikapo nyale,+ maguwa ansembe,+ ndi ziwiya+ za m’malo oyerawo zimene anali kutumikira nazo, ndiponso nsalu yotchinga,+ komanso ntchito zonse zokhudza utumikiwu.
27 Mwa ana a Kohati, panali banja la Aamuramu, banja la Aizara, banja la Aheburoni ndi banja la Auziyeli. Awa ndiwo anali mabanja a Akohati.+
28 Amuna onse owerengedwa, kuyambira amwezi umodzi kupita m’tsogolo, analipo 8,600. Ntchito ya amenewa inali kutumikira pamalo oyera.+
31 Ntchito yawo+ inali yosamalira likasa,+ tebulo,+ choikapo nyale,+ maguwa ansembe,+ ndi ziwiya+ za m’malo oyerawo zimene anali kutumikira nazo, ndiponso nsalu yotchinga,+ komanso ntchito zonse zokhudza utumikiwu.