Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yoswa 2:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Tsopano Yoswa mwana wa Nuni anatumiza amuna awiri mwachinsinsi monga azondi kuchokera ku Sitimu.+ Anawalangiza kuti: “Pitani, mukazonde dzikolo ndi mzinda wa Yeriko.” Chotero iwo anapita n’kukafika kunyumba ya mayi wina yemwe anali hule, dzina lake Rahabi,+ n’kukhala kumeneko.

  • Mateyu 1:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Salimoni anabereka Boazi, ndipo mayi ake anali Rahabi.+

      Boazi anabereka Obedi, ndipo mayi ake anali Rute.+

      Obedi anabereka Jese.+

  • Aheberi 11:31
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 31 Mwa chikhulupiriro, Rahabi+ hule lija, sanawonongedwe limodzi ndi anthu amene anachita zinthu mosamvera, chifukwa iye analandira azondi mwamtendere.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena