12 Choncho pa nthawi imeneyo tinatenga dzikoli kukhala lathu. Mafuko a Rubeni ndi Gadi+ ndinawapatsa Aroweli,+ mzinda umene uli m’chigwa cha Arinoni, ndi hafu ya dera lamapiri la Giliyadi, ndi mizinda yake.
26 Pamene Aisiraeli anali kukhala ku Hesiboni ndi m’midzi yake yozungulira,+ ku Aroweli+ ndi m’midzi yake yozungulira ndi m’mizinda yonse ya m’gombe la Arinoni kwa zaka 300, n’chifukwa chiyani simunawalande mizindayo pa nthawi imeneyo?+