Numeri 21:26 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 26 Anayamba kukhala kumeneko chifukwa Hesiboni unali mzinda wa Sihoni.+ Sihoni inali mfumu ya Aamori,+ ndipo iye ndiye anamenyana ndi mfumu ya Mowabu m’mbuyomo, n’kulanda dziko lonse limene linali m’manja mwake mpaka kuchigwa cha Arinoni.+ Deuteronomo 3:6 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 Yonseyo tinaiwononga,+ monga mmene tinachitira ndi Sihoni mfumu ya Hesiboni, mwa kuwononga mzinda uliwonse, amuna, akazi ndi ana aang’ono.+
26 Anayamba kukhala kumeneko chifukwa Hesiboni unali mzinda wa Sihoni.+ Sihoni inali mfumu ya Aamori,+ ndipo iye ndiye anamenyana ndi mfumu ya Mowabu m’mbuyomo, n’kulanda dziko lonse limene linali m’manja mwake mpaka kuchigwa cha Arinoni.+
6 Yonseyo tinaiwononga,+ monga mmene tinachitira ndi Sihoni mfumu ya Hesiboni, mwa kuwononga mzinda uliwonse, amuna, akazi ndi ana aang’ono.+