Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 33:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Tsopano Yakobo ananyamuka ulendo wopita ku Sukoti.+ Kumeneko anamanga nyumba yake ndi makola a ziweto zake.+ N’chifukwa chake malowo anawatcha kuti Sukoti.*

  • Oweruza 8:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Ndiyeno iye anapempha amuna a ku Sukoti+ kuti: “Chonde, patsaniko anthu amene akunditsatirawa+ mitanda yobulungira ya mkate chifukwa ndi otopa, pakuti ndikuthamangitsa Zeba+ ndi Zalimuna,+ mafumu a Midiyani.”

  • 1 Mafumu 7:46
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 46 Mfumuyo inaumbira zinthu zimenezi m’chikombole chadongo, m’Chigawo* cha Yorodano,+ pakati pa Sukoti+ ndi Zeretani.+

  • Salimo 60:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Pokhala woyera, Mulungu walankhula kuti:+

      “Ndidzakondwa ndi kupereka Sekemu ngati gawo la cholowa.+

      Ndipo ndidzayezera anthu anga chigwa cha Sukoti.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena