Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Oweruza 20:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Amuna ogwira lupanga a mu Isiraeli amene anasonkhanitsidwa pamodzi anali 400,000,+ kupatulapo amuna a m’dera la Benjamini. Aliyense wa amenewa anali mwamuna wankhondo.

  • 2 Samueli 24:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Tsopano Yowabu anapereka chiwerengero chonse+ cha anthu kwa mfumu. Aisiraeli analipo 800,000, amuna amphamvu ogwira lupanga, ndipo amuna a Yuda analipo 500,000.+

  • 2 Mafumu 3:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Mfumu ya Mowabu itaona kuti nkhondo yaikulira, nthawi yomweyo inatenga amuna 700 amalupanga pofuna kudutsa kuti ikapeze mfumu ya Edomu,+ koma iwo analephera.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena