Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Oweruza 11:30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 Ndiyeno Yefita analonjeza+ Yehova kuti: “Ngati mudzaperekadi ana a Amoni m’manja mwanga,

  • Oweruza 11:31
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 31 ine ndidzapereka kwa Yehova+ aliyense amene adzatuluka m’nyumba yanga kudzandichingamira pamene ndikubwera mwamtendere+ kuchokera kwa ana a Amoni. Ndidzam’pereka monga nsembe yopsereza.”+

  • Aefeso 6:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Ananu, muzimvera makolo anu+ mwa+ Ambuye, pakuti kuchita zimenezi n’chilungamo.+

  • Akolose 3:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Ananu, muzimvera+ makolo anu pa zinthu zonse, pakuti kuchita zimenezi kumakondweretsa Ambuye.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena