Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 18:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Pakati panu pasapezeke munthu wotentha mwana wake pamoto,*+ wolosera,+ wochita zamatsenga,+ woombeza,*+ wanyanga,+

  • 1 Samueli 1:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Mwanayo atangosiya kuyamwa, Hana anapita naye ku Silo atatenga ng’ombe yaing’ono yamphongo yazaka zitatu, ufa wokwana muyezo umodzi wa efa* ndi mtsuko waukulu wa vinyo.+ Iye analowa m’nyumba ya Yehova ku Silo,+ ndipo mwanayo anali naye limodzi.

  • 1 Samueli 1:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Ndipo ine ndikum’pereka* kwa Yehova.+ Ndam’pereka kwa Yehova masiku onse a moyo wake.”

      Pamenepo iye* anagwada n’kuwerama mpaka nkhope yake pansi pamaso pa Yehova.+

  • Salimo 66:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Ndidzalowa m’nyumba yanu ndi nsembe zopsereza zathunthu.+

      Ine ndidzakwaniritsa malonjezo anga kwa inu+

  • Yeremiya 7:31
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 31 Iwo amanga malo okwezeka ku Tofeti,+ m’chigwa cha mwana wa Hinomu,+ kuti azitentha ana awo aamuna ndi ana awo aakazi pamoto,+ chinthu chimene sindinawalamule kuchita ndiponso chimene sindinachiganizirepo mumtima mwanga.’+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena