Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 4:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Abele nayenso anabweretsa ana oyamba+ a nkhosa zake n’kuwapereka nsembe, ndipo anaperekanso nsembe mafuta a nkhosazo.+ Yehova anakondwera ndi Abele ndipo analandira nsembe yake,+

  • Oweruza 13:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Poyankha, mngelo wa Yehova anauza Manowa kuti: “Ngakhale mundichedwetse sindidya mkate wanu. Koma ngati mungathe kupereka kwa Yehova nsembe yopsereza,+ perekani.” Manowa ananena zimenezi chifukwa sanadziwe kuti anali mngelo wa Yehova.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena