Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 21:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Ndiyeno Mulungu anamutsegula maso Hagara, moti anaona chitsime cha madzi.+ Chotero iye anapita pachitsimecho n’kutungira madziwo m’thumba lachikopa lija, n’kumupatsa mnyamatayo kuti amwe.

  • Ekisodo 17:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Tamvera! Ine ndidzatsogola kukaima pathanthwe ku Horebe.* Kumeneko ukamenye thanthwelo, ndipo padzatuluka madzi amene anthu adzamwa.”+ Chotero Mose anachitadi zomwezo, pamaso pa akulu a Isiraeli,

  • Mateyu 19:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Yesu anawayang’anitsitsa n’kunena kuti: “Kwa anthu zimenezi n’zosathekadi, koma zinthu zonse n’zotheka kwa Mulungu.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena