Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 32:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Ngati ndikanati sindikuopa kusautsidwa ndi mdani,+

      Kuti adani awo angamve molakwa,+

      Kutinso anganene kuti: “Dzanja lathu lapambana,+

      Ndipo si Yehova amene wachita zonsezi.”+

  • Oweruza 13:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Pakuti udzatenga pakati ndi kubereka mwana wamwamuna. M’mutu mwake musadzadutse lezala+ chifukwa mwanayo adzakhala Mnaziri+ wa Mulungu potuluka m’mimba.+ Iye adzakhala patsogolo populumutsa Isiraeli m’manja mwa Afilisiti.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena