Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yoswa 15:62
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 62 Nibisani, Mzinda wa Mchere, ndi Eni-gedi.+ Mizinda 6 ndi midzi yake.

  • 2 Mbiri 20:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Choncho anthu anapita kukamuuza Yehosafati kuti: “Kwabwera khamu lalikulu la anthu ochokera kuchigawo cha kunyanja,* ku Edomu,+ kudzamenyana nanu. Panopa iwo ali ku Hazazoni-tamara, kapena kuti ku Eni-gedi.”+

  • Nyimbo ya Solomo 1:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Kwa ine, wachikondi wanga ali ngati duwa lofiirira+ m’minda ya mpesa ya ku Eni-gedi.”+

  • Ezekieli 47:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 “Asodzi adzaimirira m’mbali mwa nyanjayo kuchokera ku Eni-gedi+ mpaka ku Eni-egilaimu. Kumeneko kudzakhala malo oyanikapo makoka. Nsombazo zidzakhala zambirimbiri, zamitundu yosiyanasiyana ngati nsomba za ku Nyanja Yaikulu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena