Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 34:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 “‘Malire anu a kumadzulo+ akatsatire gombe la Nyanja Yaikulu.

  • Yoswa 23:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Taonani, ndinakupatsani malo a mitundu yonse imene yatsalayi mwa kuchita maere.+ Ndinakupatsaninso malo a mitundu imene ndinaiwononga+ kuchokera kumtsinje wa Yorodano, mpaka kolowera dzuwa, ku Nyanja Yaikulu, monga cholowa cha mafuko anu.+

  • Ezekieli 48:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Malire a kum’mwera a dzikolo akhale malire a gawo la fuko la Gadi a mbali ya kum’mwera. Malirewo achokere ku Tamara+ kukafika kumadzi a Meribati-kadesi,+ kuchigwa+ cha Iguputo, mpaka ku Nyanja Yaikulu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena