Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 26:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Davideyo anawonjezera kuti: “N’chifukwa chiyani inu mbuyanga mukuthamangitsa ine mtumiki wanu?+ Ndachita chiyani ine, ndipo ndalakwa chiyani?+

  • Salimo 7:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Inu Yehova Mulungu wanga, ngati ndachita cholakwa chilichonse,+

      Ngati manja anga achita zosalungama zilizonse,+

  • Salimo 35:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Iwo andikumbira mbuna popanda chifukwa ndi kuikapo ukonde,+

      Akumba mbunazo kuti ndigweremo ngakhale kuti sindinalakwe.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena