Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 24:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Ndiyeno Davide anauza Sauli kuti: “N’chifukwa chiyani mukumvera mawu a anthu,+ akuti, ‘Davide akufuna kukuvulazani’?

  • 1 Samueli 24:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Tsopano, bambo anga,+ onani. Taonani kansalu ka m’munsi mwa malaya anu akunja odula manja. Pakuti mmene ndinali kudula kansalu kameneka sindinakupheni. Ndiyetu dziwani ndi kuona kuti ndilibe maganizo oipa+ kapena oukira, ndipo sindinakuchimwireni, ngakhale kuti inuyo mukufunafuna moyo wanga kuti mundiphe.+

  • Salimo 7:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Inu Yehova Mulungu wanga, ngati ndachita cholakwa chilichonse,+

      Ngati manja anga achita zosalungama zilizonse,+

  • Yohane 10:32
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 32 Yesu anawauza kuti: “Ndakuonetsani ntchito zambiri zabwino zochokera kwa Atate. Tsopano mukundiponya miyala chifukwa cha ntchito iti mwa zimenezi?”

  • Yohane 18:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Yesu anamuyankha kuti: “Ngati ndalankhula molakwika, pereka umboni wa cholakwikacho. Koma ngati ndalankhula moyenera, n’chifukwa chiyani ukundimenya?”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena