Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 30:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Davide analanditsa zonse zimene Aamaleki anatenga,+ n’kulanditsanso akazi ake awiri aja.

  • Salimo 34:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Masoka a munthu wolungama ndi ochuluka,+

      Koma Yehova amamupulumutsa ku masoka onsewo.+

  • Miyambo 11:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Wolungama ndi amene amapulumutsidwa ku zowawa,+ ndipo woipa amalowa m’malo mwake.+

  • Miyambo 24:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 pakuti wolungama akhoza kugwa ngakhale nthawi 7 ndipo ndithu adzadzukanso.+ Koma anthu oipa, tsoka lidzawapunthwitsa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena