Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Amosi 6:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Ndipo m’bale wa bambo ake a mwamuna mmodzi mwa amuna ophedwawo adzawatulutsa ndi kuwatentha mmodzi ndi mmodzi kuti atulutse mafupa onse m’nyumbamo.+ Ndiyeno adzafunsa aliyense amene ali m’chipinda chamkatikati kuti, ‘Kodi muli anthu enanso mmenemo?’ Pamenepo amene ali m’chipindayo adzayankha kuti, ‘Mulibe!’ Kenako adzamuuza kuti, ‘Khala chete! Pakuti ino si nthawi yotchula dzina la Yehova.’”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena