Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Samueli 2:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Tsopano Yowabu analiza lipenga la nyanga ya nkhosa,+ ndipo anthu onse anaima, moti sanapitirizenso kuthamangitsa Isiraeli. Iwo sanayambirenso kumenyana.

  • 2 Samueli 18:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Tsopano Yowabu analiza lipenga la nyanga ya nkhosa+ kuti anthu abwerere, kusiya kuthamangitsa Isiraeli. Chotero Yowabu analetsadi anthuwo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena