-
Genesis 49:1Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
49 Pambuyo pake, Yakobo anaitana ana ake n’kuwauza kuti: “Sonkhanani pamodzi kuti ndikuuzeni zimene zidzachitika kwa inu m’masiku am’tsogolo.
-