Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 15:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Zitatero, Samueli anamuuza kuti: “Yehova wang’amba+ ndi kuchotsa ufumu wa Isiraeli kwa iwe lero, ndipo adzaupereka kwa mnzako, munthu woyenerera kuposa iwe.+

  • 1 Samueli 28:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Yehova achitadi zimene ananena kudzera mwa ine, ndipo Yehova ang’amba ufumuwu kuuchotsa kwa iwe+ ndi kuupereka kwa mnzako Davide.+

  • 1 Mbiri 12:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Tsopano nazi ziwerengero za atsogoleri a anthu okonzekera kumenya nkhondo amene anabwera kwa Davide ku Heburoni,+ kudzam’patsa ufumu+ wa Sauli malinga ndi lamulo la Yehova.+

  • Salimo 78:70
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 70 Choncho anasankha Davide mtumiki wake,+

      Ndipo anamuchotsa kumakola a nkhosa.+

  • Salimo 89:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Ndapeza Davide mtumiki wanga,+

      Ndipo ndamudzoza ndi mafuta anga opatulika.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena