Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Samueli 15:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Pamenepo mfumu inapitiriza kuuza Zadoki wansembe kuti: “Iwe ndi wamasomphenya,*+ si choncho kodi? Bwerera kumzinda mu mtendere. Bwerera pamodzi ndi Ahimazi mwana wako wamwamuna ndi Yonatani+ mwana wamwamuna wa Abiyatara. Mubwerere ndi ana anu awiri amene muli nawowa.

  • 1 Mbiri 6:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Ahitubu anabereka Zadoki,+ Zadoki anabereka Ahimazi,+

  • 1 Mbiri 6:53
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 53 Ahitubu anabereka Zadoki,+ ndipo Zadoki anabereka Ahimazi.+

  • 1 Mbiri 18:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Zadoki+ mwana wa Ahitubu ndi Ahimeleki+ mwana wa Abiyatara anali ansembe, pamene Savisa+ anali mlembi.

  • 1 Mbiri 24:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Davide ndi Zadoki,+ yemwe anali wochokera mwa ana a Eleazara, ndiponso Ahimeleki,+ wochokera mwa ana a Itamara, anagawa ana a Aroniwo m’magulu a udindo pa utumiki wawo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena