Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Samueli 13:39
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 39 Pamapeto pake mfumu Davide inalakalaka kupita kwa Abisalomu, pakuti anali atadzitonthoza pambuyo pa imfa ya Aminoni.

  • 2 Samueli 18:33
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 33 Pamenepo mfumu inasokonezeka ndipo inakwera m’chipinda cha padenga+ cha pachipata ndi kuyamba kulira. Mfumu inali kuyenda n’kumanena kuti: “Mwana wanga Abisalomu, mwana wanga, mwana wanga+ Abisalomu! Haa! Zikanakhala bwino ndikanafa ndine m’malo mwa iwe, Abisalomu mwana wanga, mwana wanga!”+

  • 2 Samueli 19:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Choncho tsiku limenelo chipulumutso chinasanduka nthawi yoti anthu onse alire maliro, chifukwa tsiku limenelo anthu anamva kuti: “Mfumu yakhumudwa ndi imfa ya mwana wake.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena